Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 150
  • Mkate Wochokera Kumwamba

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mkate Wochokera Kumwamba
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Kodi Munalawako Chakudya Chopatsa Moyo?
    Nsanja ya Olonda—2014
  • “Mkate Wowona Wakumwamba”
    Munthu Wamkulu Woposa Onse Amene Anakhalako
  • Yesu—“Mkate Wowona Wochokera Kumwamba”
    Nsanja ya Olonda—1987
  • Kristu Chitsanzo Chathu
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 150

Nyimbo 150

Mkate Wochokera Kumwamba

(Yohane 6:51)

1. Atate wakumwamba,

Simusintha nthaŵi zonse,

Tiimba zitamando

Kuyeretsa dzina lanu.

Monga Mbusa wokonda,

Munatsogolera

Anthu anu akale,

Munapatsa mana.

Munawapatsa madzi,

Ndi kuthetsa ludzu lawo.

Anadza ku Kanani,

Ali okhuta okondwa.

2. Mana munawadyetsa

Anaimira Mwana’nu,

Anachoka kumwamba

Kudzawombolatu anthu.

Iye ndiye mkatewo;

Wochoka kumwamba

Anapereka nsembe,

Kutipulumutsa.

M’chikhulupiro tidye

Mkate M’lungu watipatsa;

E, nthaŵi zonse tidye,

Kuti tikhale oyera.

3. Mbiri ya mkate uwu

Tisabisire anjala,

Pokhalatu ndi nthaŵi,

Tidyetse ‘tinkhosa’ tonse.

Thandizani enawo

Kupeza cho’nadi,

Kuti apulumuke,

Ndi kudalitsidwa.

Pa Mbuyo pa nkhondoyo

Yaikulu Armagedo,

Tidzaimba kosatha,

Zitamando za Mulungu.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena