Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 205
  • Kristu Chitsanzo Chathu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kristu Chitsanzo Chathu
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Mkate Wochokera Kumwamba
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Khristu Ndi Chitsanzo Chathu
    Imbirani Yehova
  • Tiyamika Wotipatsa Moyo
    Imbirani Yehova Zitamando
  • “Ndifuna”
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 205

Nyimbo 205

Kristu Chitsanzo Chathu

(1 Petro 2:21)

1. Nchikondi chotani Yehova asonya,

Kutumi zira Mwanake!

Kristu monga Mkate, Kuti anthu adye

Kupeza moyo wosatha.

2. Kristu anasonya Njira yopemphera:

‘Dzinalo liyeretsedwe.

Ufumuwo udze. Chifuniro chanu

Chichitidwe pansi pano.’

3. Anaphunzitsatu Cho’nadi mwachangu

Kwa omvera mawu ake.

Nafera pamtengo Kuombo la anthu

Kukwanitsa mawu a Ya.

4. Tikayamikira Nsembeyo ya Yesu,

Tiri onga ngati “nkhosa.”

Titamande M’lungu Nthaŵi zonse, ndipo,

Ndi Kristu, tipeze mphotho.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena