Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 157
  • Lambirani Yehova mu Unyamata

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Lambirani Yehova mu Unyamata
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Choloŵa Chamtengo Wapatali Kwambiri pa Zonse
    Nsanja ya Olonda—2004
  • Lambirani Yehova Mudakali Achinyamata
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Achichepere Achimwemwe mu Utumiki wa Yehova
    Nsanja ya Olonda​—1990
  • Tamandani Woyamba Kubadwa wa Yehova!
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 157

Nyimbo 157

Lambirani Yehova mu Unyamata

(Mlaliki 12:1)

1. Mkamwa mwa ana munatuluka

Mawu akutamandadi Yesu.

Inde, ana atamanda M’lungu,

Mogwirizana ndi akuluwo.

2. Makolo okonda chowonadi,

Aphunzitsa ana kuwopa Ya.

Oima kumbali ya Mulungu.

Ananu, mverani akondwere.

3. Anyamata, khalani oyera;

Phunzirani kudalira M’lungu.

Peŵani mayanjano oipa,

Aipitsa mkhalidwe wabwino.

4. Ngati ukumbuka M’lungu wako,

Kumtumikira muchowonadi,

Utakula udzasangalala,

Ndi kukondweretsa mtima wa Ya.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena