Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 181
  • Gwirizanani Nawo m’Nyimbo Yaufumu!

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Gwirizanani Nawo m’Nyimbo Yaufumu!
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Tiyeni Tiimbe Nyimbo ya Ufumu!
    Imbirani Yehova
  • Tiimbile Limodzi Nyimbo ya Ufumu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Imbani Nyimbo ya Chisangalalo Chaufumu
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Nyimbo kwa Yehova
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 181

Nyimbo 181

Gwirizanani Nawo m’Nyimbo Yaufumu!

(Salmo 98:1)

1. Pali nyimbo, nyimbo yachilakiko;

Itamanda Wam’mwambamwambayo.

Mawuwo apatsa chiyembekezo.

Imba nafe; Sangalalanitu:

‘Ya ndi Mfumu; Kondwerani.

Miyambanu, Fuulani,’

Nyimbo iyi; Idziŵitsa za Kristu

Onse atamande ufumuwo.

2. Ndi nyimboyi tilengeza Ufumu.

Yesu Kristu; alamula dziko.

Monenedweratu mtundu wabadwa,

Mwana wa Yehova alamula.

‘Mgwadireni Pampandowo.

Ndi Mfumudi. Tidziŵitse!

Phunzirani nyimbo ya Ufumuyi;

Gwadirani Ya ndi kufupidwa.’

3. Nyimboyi odzichepetsa adziŵa.

Njosavuta, njosangalatsadi.

M’dziko lonse khamu laiphunzira,

Nawonso amaitana ena:

‘Lambirani. Mtamandeni,

Adzautsa Akufawo.’

Imbani nafe zitamando za Ya.

Nyimboyi iri yosangalatsa.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena