Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • jt tsamba 32
  • Chiitano Chathu kwa Inu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Chiitano Chathu kwa Inu
  • Mboni za Yehova—Kodi Iwo Ndani? Kodi Amakhulupirira Chiyani?
  • Nkhani Yofanana
  • Fulumizanani ku Chikondano ndi Ntchito Zabwino—MotanI?
    Nsanja ya Olonda—1995
  • Khalani Okonzeka kaamba ka Mtsogolo Mwabwino
    Galamukani!—1995
  • “Mzimu ndi Mkwatibwi Akunenabe Kuti: ‘Bwera!’”
    Nsanja ya Olonda—2010
  • Chifukwa Chake Mufunikira Kufika Pamisonkhano Yachikristu
    Nsanja ya Olonda—1993
Onani Zambiri
Mboni za Yehova—Kodi Iwo Ndani? Kodi Amakhulupirira Chiyani?
jt tsamba 32

Chiitano Chathu kwa Inu

Tasangalala kulankhula nanu kudzera m’kabuku kano. Tikhulupirira kuti inunso mwasangalala kudziŵa zambiri zokhudza Mboni za Yehova. Chonde, bwerani mudzacheze nafe ku Nyumba ya Ufumu ya kwathu kuno. Dzaoneni mmene misonkhano yathu imachitikira. Dzaoneni mmene timauzira ena za uthenga wabwino wonena za dziko laparadaiso mu Ufumu wa Kristu.

Limenelo ndi lonjezo la Mulungu. “Monga mwa lonjezano lake tiyembekezera miyamba yatsopano, ndi dziko latsopano mmenemo mukhalitsa chilungamo.” (2 Petro 3:13) Papita zaka mazanamazana. Nthaŵi yodikira ikutha tsopano. Mikhalidwe ya m’dziko imasonyeza zimenezo.

“Monga momwe muona tsiku lilikuyandikira,” anatero mtumwi Paulo, “tiganizirane wina ndi mnzake kuti tifulumizane ku chikondano ndi ntchito zabwino, osaleka kusonkhana kwathu pamodzi.” (Ahebri 10:24, 25) Tikukulimbikitsani kumvera uphungu wa Paulo mwa kumasonkhana nafe.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena