Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • yp2 tsamba 56-57
  • Kusintha kwa Thupi

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kusintha kwa Thupi
  • Mayankho a Zimene Achinyamata Amafunsa, Buku Lachiwiri
  • Nkhani Yofanana
  • Zimene Zingakuthandizeni Mukatha Msinkhu
    Zimene Achinyamata Amafunsa
  • Kodi Thupi Langali Latani?
    Mayankho a Zimene Achinyamata Amafunsa, Buku Lachiwiri
  • ‘Kodi Chikuchitika N’chiyani M’thupi Mwangamu?’
    Galamukani!—2004
  • Kodi Nchiyani Chikuchitika ku Thupi Langa?
    Galamukani!—1990
Onani Zambiri
Mayankho a Zimene Achinyamata Amafunsa, Buku Lachiwiri
yp2 tsamba 56-57

Chigawo 2

Kusintha kwa Thupi

Kodi simukusangalala ndi mmene thupi lanu likusinthira?

□ Inde □ Ayi

Kuchokera pamene thupi lanu linayamba kusintha, kodi munayamba kusokonezeka maganizo, kuchita mantha kapena kumva kuti muli nokha?

□ Inde □ Ayi

Kodi tsiku lililonse mumatha nthawi yaitali mukuganizira za mnyamata kapena mtsikana winawake?

□ Inde □ Ayi

Musadandaule ngati pali funso limene mwayankha kuti “inde” pa mafunso amenewa, ndipo musaganize kuti muli ndi vuto. Dziwani kuti mukamakula, thupi lanu limasintha ndipo zimenezi zimachititsa kuti nthawi zina muzisangalala kwambiri kapena muzikhumudwa kwambiri. N’zodziwikiratu kuti muli mwana munkafuna mutakhala wamkulu, koma panopo mukuchita mantha ndi mmene thupi lanu likusinthira. Mitu 6 mpaka 8 ikuthandizani kudziwa zochita pankhaniyi.

[Chithunzi chachikulu pamasamba 56, 57]

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena