Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 27
  • Khalani ku Mbali ya Yehova

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Khalani ku Mbali ya Yehova
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Khalani Kumbali ya Yehova
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Imani ndi Yehova!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Moyo Wopanda Mapeto—Potsiriza!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Tadzipereka kwa Mulungu
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 27

Nyimbo 27

Khalani ku Mbali ya Yehova

Losindikizidwa

(Eksodo 32:26)

1. Kale tinalitu achisoni,

Pokhala m’chipembedzo chonyenga;

Koma tinasangalala zedi

Titamva za Ufumu.

(KOLASI)

Yenda ndi Yehova

Umunyadire.

Khala mbali yake

Sangakusiye.

Lengeza uthenga

Wamtenderewu.

Ufumu wa Khristu

Sudzatha konse.

2. Tsopano tikusangalaladi

Ndi kufesa mbewu za cho’nadi.

Dzina la Yehova kukwezadi

Limodzi ndi abale.

(KOLASI)

Yenda ndi Yehova

Umunyadire.

Khala mbali yake

Sangakusiye.

Lengeza uthenga

Wamtenderewu.

Ufumu wa Khristu

Sudzatha konse.

3. Mdyerekezi sitidzamuopa,

Ife timadalira Yehova.

Adani akhoza kuchuluka,

M’lungu ndi mphamvu yathu.

(KOLASI)

Yenda ndi Yehova

Umunyadire.

Khala mbali yake

Sangakusiye.

Lengeza uthenga

Wamtenderewu.

Ufumu wa Khristu

Sudzatha konse.

(Onaninso Sal. 94:14; Miy. 3:5, 6; Aheb. 13:5.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena