Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 33
  • Musawaope!

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Musawaope!
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Musawaope
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Musawaope!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • “Mawonekedwe a Dziko Lino Akusintha”
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Moyo Wopanda Mapeto—Potsiriza!
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 33

Nyimbo 33

Musawaope!

Losindikizidwa

(Mateyo 10:28)

1. Pitanibe anthu anga,

Mulalike uthenga.

Musaope adani.

Anthu onse adziwe

Kuti Mwana wanga Yesu,

Wagwetsadi mdaniyo,

Posachedwa adzam’manga,

Sadzavutitsa anthu.

(KOLASI)

Musaope anthu anga,

Kaya akuopseni.

Ndidzakusamalirani

Monga mwana wa m’diso.

2. Kaya adani n’ngambiri,

Kaya amwetulire

Mwanjira yachinyengo,

Pokusocheretsani.

Musaope anthu anga,

Kaya akuzunzeni,

Ndidzakusamalirani

Mpaka ndiwagonjetsa.

(KOLASI)

Musaope anthu anga,

Kaya akuopseni.

Ndidzakusamalirani

Monga mwana wa m’diso.

3. Sindingakuiwaleni

Ndine Mtetezi wanu.

Ngakhale akupheni,

Ndidzagonjetsa imfa.

Musaope opha thupi

Sangawononge moyo.

Inde, khulupirikani

Mudzalandira mphoto.

(KOLASI)

Musaope anthu anga,

Kaya akuopseni.

Ndidzakusamalirani

Monga mwana wa m’diso.

(Onaninso Deut. 32:10; Neh. 4:14; Sal. 59:1; 83:2, 3.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena