Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 110
  • Ntchito Zodabwitsa za Mulungu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ntchito Zodabwitsa za Mulungu
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Ntchito Zodabwitsa za Mulungu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Ntchito Zazikulu ndi Zodabwitsa za Mulungu
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Yehova Amatidziŵa Bwino!
    Nsanja ya Olonda​—1990
  • Kodi Mulungu Amakudziŵanidi?
    Nsanja ya Olonda—1993
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 110

Nyimbo 110

Ntchito Zodabwitsa za Mulungu

Losindikizidwa

(Salimo 139)

1. Inu Mulungu mumadziwa

Ndikagona ndipo ndikadzuka.

Mumadziwanso maganizo anga

Ngakhale mawu anga

Ndi njira zanga.

Munaona malo ’bisika.

Panthawi yomwe ndinali m’mimba.

Ziwalo zangatu zinalembedwa,

Ndikutamandani ndinu wodabwitsa.

Nzeru zanu Mulungu n’zodabwitsa.

Zimenezi ndithu ndikudziwa.

Ndikaopa kuphimbidwa ndi mdima

Mzimu wanu M’lungu undipeza.

N’kuti komwe ndingabisale

Komwe inu simungandione?

Kumwamba kodi kapena kumanda,

Mumdima, m’nyanja?

Ayi ndithu kulibe.

(Onaninso Sal. 66:3; 94:19; Yer. 17:10.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena