Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 5
  • Ntchito Zodabwitsa za Mulungu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ntchito Zodabwitsa za Mulungu
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Ntchito Zodabwitsa za Mulungu
    Imbirani Yehova
  • Ntchito Zazikulu ndi Zodabwitsa za Mulungu
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Tinapangidwa Modabwitsa Kwambiri
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
  • Yehova Amatidziŵa Bwino!
    Nsanja ya Olonda​—1990
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 5

NYIMBO 5

Ntchito Zodabwitsa za Mulungu

Losindikizidwa

(Salimo 139)

  1. 1. M’lungu mumandidziwa bwino

    Ndikagona kaya ndikadzuka.

    Mumafufuza maganizo anga.

    Mumadziwanso zimene

    Ndimachita.

    Munandiona ndili m’mimba,

    Munaonanso mafupa anga.

    Munapanga ziwalo zanga zonse.

    M’lungu wamphamvu

    Ndizikutamandani.

    Nzeru zanu Mulungu n’zodabwitsa,

    Ndikudziwa ndithu zimenezi.

    Ngakhale nditabisidwa ndi mdima

    Mzimu wanu udzandipezabe.

    Kodi ndingabisale kuti

    Komwe inu simungandione,

    Kumanda kodi kapena kumwamba?

    Palibe malo

    Omwe ndingabisale.

(Onaninso Sal. 66:3; 94:19; Yer. 17:10.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena