Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb16 September tsamba 5
  • Tinapangidwa Modabwitsa Kwambiri

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tinapangidwa Modabwitsa Kwambiri
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
  • Nkhani Yofanana
  • ‘Tinapangidwa Modabwitsa’
    Nsanja ya Olonda—2007
  • Yehova Amatidziŵa Bwino!
    Nsanja ya Olonda​—1990
  • Kodi Mulungu Amakudziŵanidi?
    Nsanja ya Olonda—1993
  • Mulungu Amakumvetsani
    Nsanja ya Olonda—2014
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
mwb16 September tsamba 5

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | MASALIMO 135-141

Tinapangidwa Modabwitsa Kwambiri

Davide ankaganizira za makhalidwe a Mulungu omwe amaonekera m’zinthu zimene analenga. Zimenezi zinachititsa kuti azitumikira Yehova ndi mtima wonse.

Mayi woyembekezera ndi mwamuna wake

Davide atayamba kuganizira mozama zinthu zimene Yehova analenga, anayamba kutamanda Yehova

139:14

  • “Ndidzakutamandani chifukwa munandipanga modabwitsa”

139:15

  • “Mafupa anga sanali obisika kwa inu pamene munali kundipanga m’malo obisika, pamene munali kundiwomba ngati nsalu m’malo apansi kwambiri padziko lapansi”

139:16

  • “Maso anu anandiona pamene ndinali mluza, ndipo ziwalo zanga zonse zinalembedwa m’buku lanu”

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena