Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 46
  • Yehova ndi Mfumu Yathu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Yehova ndi Mfumu Yathu
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Yehova Ndi Mfumu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • ‘Yehova Iye Mwini Wakhala Mfumu!’
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Ufumu Umene Ukulamulira Kumwamba Ubwere
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Ufumu Umene Ukulamulira Kumwamba Ubwere
    Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 46

Nyimbo 46

Yehova ndi Mfumu Yathu

Losindikizidwa

(Salmo 97:1)

1. Kondwa, lemekeza Yehova.

Kumwamba kulengeza chilungamo.

Timuimbire Mulungu mokondwera

Pa ntchito zake zazikulu.

(KOLASI)

Kumwamba kukondwe, Dziko likondwere,

Chifukwa Yehova ndi Mfumu!

Kumwamba kukondwe, Dziko likondwere,

Chifukwa Yehova ndi Mfumu!

2. Nena za kukwezeka kwake,

Za kupulumutsa kwake kwamphamvu.

Yehova ndi Mfumu, Timutamandetu.

Tiyeni, tim’gwadire tonse.

(KOLASI)

Kumwamba kukondwe, Dziko likondwere,

Chifukwa Yehova ndi Mfumu!

Kumwamba kukondwe, Dziko likondwere,

Chifukwa Yehova ndi Mfumu!

3. Wakhazikitsatu Ufumu.

Waika Mwana wake pampandowo.

Milungu yonyenga ichite manyazi,

Ulemu wonse n’ngwa Yehova.

(KOLASI)

Kumwamba kukondwe, Dziko likondwere,

Chifukwa Yehova ndi Mfumu!

Kumwamba kukondwe, Dziko likondwere,

Chifukwa Yehova ndi Mfumu!

(Onaninso 1 Mbiri 16:9; Sal. 68:20; 97:6, 7.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena