Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • snnw tsamba 1
  • Ufumu Umene Ukulamulira Kumwamba Ubwere

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ufumu Umene Ukulamulira Kumwamba Ubwere
  • Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Nkhani Yofanana
  • Ufumu Umene Ukulamulira Kumwamba Ubwere
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Yehova Ndi Mfumu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Yehova ndi Mfumu Yathu
    Imbirani Yehova
  • Munapereka Mwana Wanu Wobadwa Yekha
    Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
Onani Zambiri
Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
snnw tsamba 1

Nyimbo 136

Ufumu Umene Ukulamulira Kumwamba Ubwere

(Chivumbulutso 11:15; 12:10)

  1. Yehova Mulungu wathu,

    Ndinu wamuyaya.

    Mwapatsa Yesu Ufumu,

    Mwa kufuna kwanu.

    Ufumu udzalamula

    Padziko lonse lapansi.

    (KOLASI)

    Zafika tsopano

    Ufumu chipulumutso.

    Ufumu ‘lamula.

    Tipempha kuti “Ubwere.”

  2. Nthawi ya Satana yatha

    Dziko latsopano

    Lili pafupi kwambiri.

    Mavuto adzatha.

    Ufumu udzalamula

    Padziko lonse lapansi.

    (KOLASI)

    Zafika tsopano

    Ufumu chipulumutso.

    Ufumu ‘lamula.

    Tipempha kuti “Ubwere.”

  3. Angelo asangalala,

    Aimba mokondwa.

    Satana wachotsedwako,

    Onse akondwera.

    Ufumu udzalamula

    Padziko lonse lapansi.

    (KOLASI)

    Zafika tsopano

    Ufumu chipulumutso.

    Ufumu ‘lamula.

    Tipempha kuti “Ubwere.”

(Onaninso Dan. 2:34, 35; 2 Akor. 4:18.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena