Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mb phunziro 5
  • Phunziro 5

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Phunziro 5
  • Zimene Ndikuphunzira M’Baibulo
  • Nkhani Yofanana
  • Mwetulirani—N’zothandiza kwa Inu!
    Galamukani!—2000
  • Ubwino wa Kumwetulira
    Galamukani!—2003
  • Tikuyamikani Yehova
    Imbirani Yehova
  • Tikuyamikani, Yehova
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Zimene Ndikuphunzira M’Baibulo
mb phunziro 5

Phunziro 5

Losindikizidwa

1 Atesalonika 5:18

Mnzako akakupatsa mphatso kapena kukuchitira zabwino umanyadira ndipo umasekerera.

Komabe nthawi zonse uzikumbukira kunena kuti “Zikomo.”

ZOTI MUCHITE

Mwana wanuyo muwerengereni:

1 Atesalonika 5:18

Muuzeni mwanayo kuti aloze:

Mphatso Mnyamata

Chitseko Chakudya

Pezani zinthu zobisika.

Apozi Telefoni

Mufunseni mwana wanu kuti:

N’chifukwa chiyani ndi bwino kunena kuti “Zikomo”?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena