Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • snnw tsamba 2
  • Tithandizeni Kukhala Olimba Mtima

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tithandizeni Kukhala Olimba Mtima
  • Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Nkhani Yofanana
  • Tithandizeni Kukhala Olimba Mtima
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • ‘Lankhulani Mawu a Mulungu Molimba Mtima’
    Nsanja ya Olonda—2010
  • Tsanzirani Yesu mwa Kulalikira Molimba Mtima
    Nsanja ya Olonda—2009
  • Kodi Mumalalikira Molimba Mtima?
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2000
Onani Zambiri
Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
snnw tsamba 2

Nyimbo 137

Tithandizeni Kukhala Olimba Mtima

(Machitidwe 4:29)

  1. Polalikira Ufumu,

    Kukweza dzina lanu.

    Anthu ena amatsutsa,

    Ndiponso kutinyoza.

    Koma sitiwaopa

    Timamvera inu nokha.

    Choncho Yehova, tikupempha

    Mutipatse mzimu wanu.

    (KOLASI)

    Polalikira uthenga,

    Mutichotsere mantha.

    Tikhale olimba mtima

    Anthu amve uthenga.

    Amagedo ikufika,

    Tikhale olimba mtima,

    Tithandizeni Yehova.

    Tikupempha.

  2. Pamene tichita mantha,

    Mudziwa ndife fumbi.

    Mudzatithandiza ndithu

    Paja munalonjeza.

    Imvani kuopseza,

    Kwa anthu odana nafe.

    Tithandizeni, tisaope.

    Tikhale olimba mtima.

    (KOLASI)

    Polalikira uthenga,

    Mutichotsere mantha.

    Tikhale olimba mtima

    Anthu amve uthenga.

    Amagedo ikufika,

    Tikhale olimba mtima,

    Tithandizeni Yehova.

    Tikupempha.

(Onaninso 1 Ates. 2:2; Aheb. 10:35.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena