Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 27
  • Ulemerero wa Ana a Mulungu Udzaonekera

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ulemerero wa Ana a Mulungu Udzaonekera
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Ulemerero wa Ana a Mulungu Udzaonekera
    Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Moyo Wopanda Mapeto—Potsiriza!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Lonjezo la Mulungu la Paradaiso
    Imbirani Yehova Zitamando
  • “Ndine Pano! Munditumize Ine”
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 27

NYIMBO 27

Ulemerero wa Ana a Mulungu Udzaonekera

Losindikizidwa

(Aroma 8:19)

  1. 1. Posachedwa M’lungu wathu,

    Adzatisonyeza

    Kuti anthu odzozedwa

    Ndi ana akedi.

    (KOLASI)

    Khristu ndi odzozedwawo

    Adzapambanadi.

    Ulemerero wawonso

    Udzaonekera.

  2. 2. Omwe atsala padziko

    Adzaitanidwa.

    Khristu Mfumu ya mafumu

    Adzatenga onse.

    (KOLASI)

    Khristu ndi odzozedwawo

    Adzapambanadi.

    Ulemerero wawonso

    Udzaonekera.

    (VESI LOKOMETSERA)

    Limodzi ndi Yesu Khristu

    Adzamenya nkhondo.

    Kenako ukwati wawo

    Udzachitikadi.

    (KOLASI)

    Khristu ndi odzozedwawo

    Adzapambanadi.

    Ulemerero wawonso

    Udzaonekera.

(Onaninso Dan. 2:​34, 35; 1 Akor. 15:​51, 52; 1 Ates. 4:​15-17.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena