Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • snnw tsamba 16
  • Ulemerero wa Ana a Mulungu Udzaonekera

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ulemerero wa Ana a Mulungu Udzaonekera
  • Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Nkhani Yofanana
  • Ulemerero wa Ana a Mulungu Udzaonekera
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Moyo Wopanda Mapeto—Potsiriza!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Lonjezo la Mulungu la Paradaiso
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Kukonzekera Kupita Kolalikira
    Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
Onani Zambiri
Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
snnw tsamba 16

Nyimbo 151

Ulemerero wa Ana a Mulungu Udzaonekera

  1. Posachedwa Mlungu wathu

    Odzozedwa ake,

    Adzawasonyeza kuti

    Ndi ana akedi.

    (KOLASI)

    Khristu ndi odzozedwawo

    Adzapambanadi.

    Ulemerero wawonso

    Udzaonekera.

  2. Posachedwa otsalira

    Adzaitanidwa.

    Khristu Mfumu ya mafumu,

    Adzatenga onse.

    (Kolasi)

    Khristu ndi odzozedwawo

    Adzapambanadi.

    Ulemerero wawonso

    Udzaonekera.

    (VESI LOKOMETSERA)

    Limodzi ndi Mbuye wawo

    Adzamenya nkhondo.

    Ukwati ndi Mbuye Yesu

    Udzachitikatu.

    (Kolasi)

    Khristu ndi odzozedwawo

    Adzapambanadi.

    Ulemerero wawonso

    Udzaonekera.

(Onaninso Dan. 2:34, 35; 1 Akor. 15:51, 52; 1 Ates. 4:15-17.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena