Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 71
  • Ndife Gulu Lankhondo la Yehova

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndife Gulu Lankhondo la Yehova
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Ndife Gulu Lankhondo la Yehova
    Imbirani Yehova
  • Pitirizani Kugwira Ntchito, Kukhala Maso ndi Kudikira
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Moyo Wopanda Mapeto—Potsiriza!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Wonani Khamu la Yehova!
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 71

NYIMBO 71

Ndife Gulu Lankhondo la Yehova

Losindikizidwa

(Aefeso 6:11-14)

  1. 1. Ndife gulu lankhondo

    La M’lungu wathu,

    Lotsogoleredwa ndi

    Mwana wake Yesu.

    Ngakhale titsutsidwe

    Sitimasiya,

    Sitiopa kanthu

    Ndife olimba.

    (KOLASI)

    Ndife gulu lankhondo.

    Tikulengeza

    Ufumu wayamba

    Kulamulira.

  2. 2. Ndife anthu a M’lungu.

    Tikufufuza

    Anthu omwe ndi nkhosa

    Zosowa za M’lungu

    Ndipo tikawapeza,

    Tiwaphunzitse,

    Tiwalimbikitse

    Tizisonkhana.

    (KOLASI)

    Ndife gulu lankhondo.

    Tikulengeza

    Ufumu wayamba

    Kulamulira.

  3. 3. Ndife gulu lankhondo

    Lomvera Yesu,

    Lokonzekera nkhondo

    Ndi lolimba mtima.

    Koma tikhale tcheru

    Kuti tisagwe,

    Zinthu zikavuta

    Tisafooke.

    (KOLASI)

    Ndife gulu lankhondo.

    Tikulengeza

    Ufumu wayamba

    Kulamulira.

(Onaninso Afil. 1:7; Filim. 2.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena