Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 75
  • “Ine Ndilipo! Nditumizeni”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Ine Ndilipo! Nditumizeni”
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • “Ine Ndilipo! Nditumizeni”
    Imbirani Yehova
  • “Ndine Pano! Munditumize Ine”
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Tidzakhala Ndi Moyo Wosatha
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Kukonzekera Kupita Kokalalikira
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 75

NYIMBO 75

“Ine Ndilipo! Nditumizeni”

Losindikizidwa

(Yesaya 6:8)

  1. 1. Anthu ena amanyoza

    Dzina loyera la M’lungu.

    Amati ali ndi nkhanza

    Kapena kulibe M‘lungu.

    Ndani akaliyeretse

    Dzina la Yehova M’lungu?

    (KOLASI 1)

    ‘Ndilipo! Nditumizeni.

    Ndikawauza za inu.

    Uwu ndi mwayi waukulu.

    Ine nditumizeni.’

  2. 2. Ena samaopa M’lungu

    Akumati akuchedwa.

    Ena samamulambira

    Amakonda Kaisara.

    Ndani akawachenjeze

    Za nkhondo ya M’lungu wathu?

    (KOLASI 2)

    ‘Ndilipo! Nditumizeni.

    Ine ndikawachenjeza.

    Uwu ndi mwayi waukulu.

    Ine nditumizeni!’

  3. 3. Anthu akudandaula,

    Zoipa zikuchuluka.

    Iwo akufunitsitsa

    Atadziwa choonadi.

    Ndani akawatonthoze?

    Ndani akawathandize?

    (KOLASI 3)

    ‘Ndilipo! Nditumizeni.

    Ndikaphunzitse ofatsa.

    Uwu ndi mwayi waukulu.

    Ine nditumizeni.’

(Onaninso Sal. 10:4; Ezek. 9:4.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena