Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 86
  • Tiziphunzitsidwa

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tiziphunzitsidwa
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Tiziphunzitsidwa Ndi Yehova
    Imbirani Yehova
  • Yendani ndi Mulungu!
    Imbirani Yehova
  • Muziyenda Ndi Mulungu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nyimbo Yatsopano
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 86

NYIMBO 86

Tiziphunzitsidwa

Losindikizidwa

(Yesaya 50:4; 54:13)

  1. 1. Bwerani mosangalala muphunzire.

    “Bwerani mumwe madzi a moyo.”

    Nonse anjala bwerani mudye

    Ndi kudzalandira malangizo.

  2. 2. Tisasiyetu kusonkhana pamodzi.

    Tiziphunzitsidwa ndi Mulungu.

    Kuno n’kumene kuli abale,

    Kuno kuli mzimu wa Mulungu.

  3. 3. Lilime lophunzitsidwa choonadi

    Limasangalatsa kulimvera.

    Tisonkhane ndi anthu a M’lungu.

    Tizipezeka pamisonkhano.

(Onaninso Aheb. 10:​24, 25; Chiv. 22:17.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena