Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 113
  • Yehova Amatipatsa Mtendere

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Yehova Amatipatsa Mtendere
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Mtendere Wathu Wamtengo Wapatali
    Imbirani Yehova
  • Kukhala Kwathu ndi Mtendere
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Lolani “Mtendere wa Mulungu” Uchinjirize Mtima Wanu
    Nsanja ya Olonda—1991
  • Mtendere Weniweni—Kodi Udzachokera Kuti?
    Nsanja ya Olonda—1997
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 113

NYIMBO 113

Yehova Amatipatsa Mtendere

Losindikizidwa

(Yohane 14:27)

  1. 1. Tamandani

    Yehova wamtendereyo.

    Wapatsa Yesu mphamvu

    zothetsa nkhondo.

    Adzakonzadi zinthu

    mwachilungamo.

    Mtendere udzakhala

    padziko lonse.

  2. 2. Tasiya kulankhula

    zokhumudwitsa.

    Malupanga, mikondo,

    zonse tataya.

    Timasunga mtendere

    pokhululuka

    Monga nkhosa za

    Yesu zamtenderedi.

  3. 3. Mtendere ndi

    umboni wa madalitso.

    Tasunga malamulo a

    M’lungu wathu.

    Timakonda mtendere.

    Tiusonyeze

    Mpaka m’Paradaiso

    wamtendereyo.

(Onaninso Sal. 46:9; Yes. 2:4; Yak. 3:​17, 18.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena