Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 159
  • Kukhala Kwathu ndi Mtendere

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kukhala Kwathu ndi Mtendere
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Mtendere Wathu Wamtengo Wapatali
    Imbirani Yehova
  • Yehova Amatipatsa Mtendere
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Lolani “Mtendere wa Mulungu” Uchinjirize Mtima Wanu
    Nsanja ya Olonda—1991
  • Kodi Adzatsogolera Anthu ku Mtendere Ndani?
    Nsanja ya Olonda​—1990
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 159

Nyimbo 159

Kukhala Kwathu ndi Mtendere

(Yohane 14:27)

1. Kwa oipa kulibe

Mtendere konse;

Ngakhaletu kukhamu

La Satanalo.

Mtendere uchokera

Kwa Yehovayo,

Umabwera kwa onse

Okonda M’lungu.

2. Tamandani Yehova

Wamtendereyo.

Athetsa nkhondo zonse,

’Gwirizanitsa.

Kalonga Wamtendere,

Kristu Mwanake.

Atalakika iye,

Mtendere udza.

3. Zonyansa zotuluka

Mkamwa tasiya.

Lupanga ndi mikondo

Ndi zolimira.

Tisungetu mtendere,

Tikhulukire.

Mwachikonditu monga

“Nkhosa” za Yesu.

4. Mtendere ndi chipatso

Chachilungamo,

Umboni wanzeruyo

Yodza kumwamba.

Yomwe tipempherera

Mtendere wathu,

Kuŵala kubweretsa

Chimwemwe chonse.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena