Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 115
  • Tizithokoza Kuleza Mtima kwa Mulungu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tizithokoza Kuleza Mtima kwa Mulungu
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Tikuthokoza Mulungu Chifukwa cha Kuleza Mtima Kwake
    Imbirani Yehova
  • Moyo Wopanda Mapeto—Potsiriza!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Imani ndi Yehova!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Kodi Mudzachita Zinthu Zosonyeza Kuyamikira Yehova pa Nyengo ya Chikumbutso Ikubwerayi?
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 115

NYIMBO 115

Tizithokoza Kuleza Mtima kwa Mulungu

Losindikizidwa

(2 Petulo 3:15)

  1. 1. Yehova Mulungu wamphamvu

    Mumakonda chilungamo.

    Ngakhale zoipa m’dziko

    Zikungochulukirabe,

    Tikudziwa simukuchedwa

    Posachedwa mudzazichotsa.

    (KOLASI)

    Tikudikira mwachidwi.

    Timatamanda dzina lanu.

  2. 2. Zaka zambiritu kwa inu

    Ndi nthawi yochepa chabe.

    Tsiku lanu lalikulu

    Layandikira kwambiri.

    Anthu ochimwa akalapa

    Mumasangalala kwambiri.

    (KOLASI)

    Tikudikira mwachidwi.

    Timatamanda dzina lanu.

(Onaninso Neh. 9:​30; Luka 15:7; 2 Pet. 3:​8, 9.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena