Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • CO-pgm17 tsamba 4-5
  • Loweruka

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Loweruka
  • Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2017
  • Nkhani Yofanana
  • Lachisanu
    Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2017
  • Loweruka
    Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2021
  • Loweruka
    Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2020
  • Lachisanu
    Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2019
Onani Zambiri
Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2017
CO-pgm17 tsamba 4-5

Loweruka

“Kondwerani ndi chiyembekezocho. Pirirani chisautso”—AROMA 12:12

M’MAWA

  • 9:20 Kuonera Vidiyo ya Nyimbo

  • 9:30 Nyimbo Na. 68 ndi Pemphero

  • 9:40 NKHANI YOSIYIRANA: Yehova ‘Amatonthoza Komanso Amapereka Mphamvu’ kwa . . .

    • Ofooka Komanso Amtima Wachisoni (Aroma 15:4, 5; 1 Atesalonika 5:14; 1 Petulo 5:7-10)

    • Anthu Ovutika (1 Timoteyo 6:18)

    • “Ana Amasiye” (Salimo 82:3)

    • Anthu Achikulire (Levitiko 19:32)

  • 10:50 Nyimbo Na. 90 ndi Zilengezo

  • 11:00 NKHANI YOSIYIRANA: Mangani Nyumba Yolimba

    • ‘Muzikhala Okhutira Ndi Zimene Muli Nazo’ (Aheberi 13:5; Salimo 127:1, 2)

    • Muziteteza Ana Anu ku “Zinthu Zoipa” (Aroma 16:19; Salimo 127:3)

    • Muziphunzitsa Ana Anu ‘M’njira Yowayenerera’ (Miyambo 22:3, 6; Salimo 127:4, 5)

  • 11:45 NKHANI YA UBATIZO: ‘Musamaope Chochititsa Mantha Chilichonse’ (1 Petulo 3:6, 12, 14)

  • 12:15 Nyimbo Na. 139 ndi Kupuma

MASANA

  • 1:35 Kuonera Vidiyo ya Nyimbo

  • 1:45 Nyimbo Na. 43

  • 1:50 NKHANI YOSIYIRANA: Muzitsanzira “Anthu Amene Anapirira”

    • Yosefe (Genesis 37:23-28; 39:17-20; Yakobo 5:11)

    • Yobu (Yobu 10:12; 30:9, 10)

    • Mwana Wamkazi wa Yefita (Oweruza 11:36-40)

    • Yeremiya (Yeremiya 1:8, 9)

  • 2:35 SEWERO: Kumbukirani Mkazi wa Loti​—Mbali Yachiwiri (Luka 17:28-33)

  • 3:05 Nyimbo Na. 75 ndi Zilengezo

  • 3:15 NKHANI YOSIYIRANA: Tingaphunzire Kupirira Kuchokera ku Zinthu za M’chilengedwe

    • Ngamila (Yuda 20)

    • Mitengo ya M’mapiri Yooneka Ngati Paini (Akolose 2:6, 7; 1 Petulo 5:9, 10)

    • Agulugufe (2 Akorinto 4:16)

    • Mbalame Zinazake za M’nyanja Zikuluzikulu (1 Akorinto 13:7)

    • Mbalame Zinazake Zolimba Mtima (Aheberi 10:39)

    • Mitengo ya Mthethe (Aefeso 6:13)

  • 4:15 Ananu, Yehova Amasangalala Mukamapirira (Miyambo 27:11)

  • 4:50 Nyimbo Na. 89 ndi Pemphero Lomaliza

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena