Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • CO-pgm20 tsamba 4-5
  • Loweruka

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Loweruka
  • Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2020
  • Nkhani Yofanana
  • Loweruka
    Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2021
  • Lamlungu
    Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2020
  • Loweruka
    Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2019
  • Lachisanu
    Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2024
Onani Zambiri
Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2020
CO-pgm20 tsamba 4-5

Loweruka

“Nyadirani dzina lake loyera. Mtima wa anthu ofunafuna Yehova usangalale”​—Salimo 105:3

M’MAWA

  • 9:20 Kuonera Vidiyo ya Nyimbo

  • 9:30 Nyimbo Na. 53 ndi Pemphero

  • 9:40 NKHANI YOSIYIRANA: Muziwonjezera Luso Lanu Kuti Muzisangalala ndi Ntchito Yophunzitsa

    • • Muzifunsa Mafunso (Yakobo 1:19)

    • • Muzigwiritsa Ntchito Mawu a Mulungu (Aheberi 4:12)

    • • Muzigwiritsa Ntchito Mafanizo (Mateyu 13:34, 35)

    • • Muziphunzitsa ndi Mtima Wonse (Aroma 12:11)

    • • Muzisonyeza Kuti Mumawaganizira (1 Atesalonika 2:7, 8)

    • • Muziwafika Pamtima (Miyambo 3:1)

  • 10:50 Nyimbo Na. 58 ndi Zilengezo

  • 11:00 NKHANI YOSIYIRANA: Muzigwiritsa Ntchito Zomwe Yehova Watipatsa Kuti Muzisangalala ndi Ntchito Yophunzitsa

    • • Zinthu Zofufuzira (1 Akorinto 3:9; 2 Timoteyo 3:16, 17)

    • • Abale Athu (Aroma 16:3, 4; 1 Petulo 5:9)

    • • Pemphero (Salimo 127:1)

  • 11:45 NKHANI YA UBATIZO: Mukabatizidwa Muzisangalala Kwambiri (Miyambo 11:24; Chivumbulutso 4:11)

  • 12:15 Nyimbo Na. 79 ndi Kupuma

MASANA

  • 1:35 Kuonera Vidiyo ya Nyimbo

  • 1:45 Nyimbo Na. 76

  • 1:50 Mmene Abale Athu Akusangalalira ndi Ntchito Yophunzitsa Anthu ku . . .

    • • Africa

    • • Asia

    • • Europe

    • • North America

    • • Oceania

    • • South America

  • 2:35 NKHANI YOSIYIRANA: Muzithandiza Amene Mukuphunzira Nawo Baibulo . . .

    • • Kuti Azidzidyetsa Mwauzimu (Mateyu 5:3; Yohane 13:17)

    • • Kuti Azipezeka Pamisonkhano (Salimo 65:4)

    • • Kuti Asamacheze ndi Anthu Olakwika (Miyambo 13:20)

    • • Kuti Asiye Makhalidwe Oipa (Aefeso 4:22-24)

    • • Kuti Akhale pa Ubwenzi ndi Yehova (1 Yohane 4:8, 19)

  • 3:30 Nyimbo Na. 110 ndi Zilengezo

  • 3:40 VIDIYO: Nehemiya: “Chimwemwe Chimene Yehova Amapereka Ndicho Malo Anu Achitetezo”​—Mbali Yoyamba (Nehemiya 1:1–6:19)

  • 4:15 Tikamaphunzitsa Anthu Tikukonzekera Kudzagwiranso Ntchitoyi M’dziko Latsopano (Yesaya 11:9; Machitidwe 24:15)

  • 4:50 Nyimbo Na. 140 ndi Pemphero Lomaliza

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena