Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • th phunziro 17 tsamba 20
  • Kulankhula Zomveka

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kulankhula Zomveka
  • Kuwerenga Komanso Kuphunzitsa Mwaluso
  • Nkhani Yofanana
  • Lankhulani Zomveka Bwino kwa Ena
    Pindulani ndi Sukulu ya Utumiki wa Mulungu
  • Nkhani Yophunzitsadi Anthu
    Kuwerenga Komanso Kuphunzitsa Mwaluso
  • Kulankhula ndi Mtima Wonse
    Kuwerenga Komanso Kuphunzitsa Mwaluso
  • Kulankhula Mokambirana ndi Anthu
    Kuwerenga Komanso Kuphunzitsa Mwaluso
Onani Zambiri
Kuwerenga Komanso Kuphunzitsa Mwaluso
th phunziro 17 tsamba 20

PHUNZIRO 17

Kulankhula Zomveka

Lemba

1 Akorinto 14:9

MFUNDO YAIKULU: Muzilankhula m’njira yoti anthu azimvetsa zimene mukunena.

MMENE MUNGACHITIRE:

  • Yesetsani kuti muidziwe bwino nkhani yanu. Mukaidziwa bwino nkhani yanu mukhoza kuifotokoza mosavuta m’mawu anuanu.

  • Muzigwiritsa ntchito ziganizo zifupizifupi zosavuta kumva. Ngakhale kuti pena mukhoza kugwiritsa ntchito ziganizo zitalizitali, muzizidula moyenerera mukamafotokoza mfundo yofunika.

    Mfundo yothandiza

    Muzichotsa timfundo tosafunika timene tikhoza kungosokoneza anthu. Mawu anu azikhala osavuta kumva okhaokha.

  • Muzifotokoza mawu ovuta. Pewani kugwiritsa ntchito mawu amene anthu sawadziwa. Muzifotokozera mawu ovuta, anthu a m’Baibulo osadziwika kwambiri komanso miyeso ndi zikhalidwe zakale.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena