Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • T-sfr tsamba 1-2
  • Kodi n’zotheka kukhala popanda zopweteka zilizonse?

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kodi n’zotheka kukhala popanda zopweteka zilizonse?
  • Kodi N’zotheka Kukhala Popanda Zopweteka Zilizonse?
  • Nkhani Yofanana
  • Kodi malangizo a Yesu ndi othandizabe masiku ano?
    Kodi Malangizo a Yesu ndi Othandizabe Masiku Ano?
  • Kodi Mulungu woona ndi ndani?
    Kodi Mulungu Woona ndi Ndani?
  • Kodi n’zotheka kukhala ndi moyo mpaka kalekale?
    Kodi N’zotheka Kukhala ndi Moyo Mpaka Kalekale?
  • Kodi Ufumu wa Mulungu udzathetsa bwanji mavuto athu?
    Kodi Ufumu wa Mulungu Udzathetsa Bwanji Mavuto Athu?
Onani Zambiri
Kodi N’zotheka Kukhala Popanda Zopweteka Zilizonse?
T-sfr tsamba 1-2
Anthu a misinkhu yosiyanasiyana akucheza mosangalala.

Kodi n’zotheka kukhala popanda zopweteka zilizonse?

Mulungu “adzapukuta misozi yonse mʼmaso mwawo ndipo imfa sidzakhalaponso. Sipadzakhalanso kulira, kubuula kapena kupweteka.”—Chivumbulutso 21:4.

Baibulo limatitsimikizira kuti

  • Mulungu si amene amachititsa mavuto athu.—Yakobo 1:13.

  • Iye amamvetsa zimene timakumana nazo ndipo adzatipulumutsa ku mavuto athu onse.—Salimo 34:​17-19.

Kuti mudziwe zambiri, pitani pa jw.org.

Kachidindo kopangira sikani.

© 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania

    Mabuku a Chichewa (1974-2026)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena