Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w12 11/1 tsamba 24-25
  • Zimene Ndikuphunzira M’Baibulo

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zimene Ndikuphunzira M’Baibulo
  • Nsanja ya Olonda—2012
  • Nkhani Yofanana
  • Phunziro 4
    Zimene Ndikuphunzira M’Baibulo
  • Mwetulirani—N’zothandiza kwa Inu!
    Galamukani!—2000
  • Tizithokoza Mulungu Chifukwa cha Mvula
    Nsanja ya Olonda—2009
  • Amene Anapanga Zinthu Zonse
    Phunzirani kwa Mphunzitsi Waluso
Onani Zambiri
Nsanja ya Olonda—2012
w12 11/1 tsamba 24-25

Zimene Ndikuphunzira M’Baibulo

ANA AZAKA ZOSAPITIRIRA ZITATU

Tsiku lina kunja kunkagwa mvula.

Tomoko anadandaula kuti:

“Ndikulephera kutuluka.

N’chifukwa chiyani mvulayi sikusiya?”

Koma kenako,

mvula ija inasiya.

Ndipo dzuwa linawala.

Tomoko anakondwera kwambiri.

Atathamangira panja,

anadabwa kwambiri

ndi zimene anaona.

Tomoko ananena kuti:

“Sindimadziwa kuti mvulayi,

yomwe ndi yochokera kwa Mulungu,

imachititsa kuti

zomera zipange maluwa.”

ZOTI MAKOLO ACHITE

Muuzeni mwana wanuyo kuti aloze:

  • Windo

  • Tomoko

  • Maluwa

  • Mbalame

  • Mtengo

Pezani zinthu zobisika izi:

  • Chikumbu

  • Ndege

Werengani Machitidwe 14:17. Kodi n’chifukwa chiyani Yehova analenga mvula?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena