Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mb phunziro 4
  • Phunziro 4

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Phunziro 4
  • Zimene Ndikuphunzira M’Baibulo
  • Nkhani Yofanana
  • Zimene Ndikuphunzira M’Baibulo
    Nsanja ya Olonda—2012
  • Mwetulirani—N’zothandiza kwa Inu!
    Galamukani!—2000
  • Tizithokoza Mulungu Chifukwa cha Mvula
    Nsanja ya Olonda—2009
  • Uyo Amene Anapanga Zinthu Zonse
    Kumamumvetsera Mphunzitsi Wamkuru’yo
Onani Zambiri
Zimene Ndikuphunzira M’Baibulo
mb phunziro 4

Phunziro 4

Losindikizidwa

Machitidwe 14:17

Tsiku lina kunja kunkagwa mvula.

Choncho Tomoko anadandaula kuti:

“Ndikulephera kutuluka.

N’chifukwa chiyani mvulayi sikusiya?”

Koma kenako,

mvula ija inasiya.

Ndipo dzuwa linawala.

Tomoko anasangalala kwambiri.

Ndiyeno anathamanga kupita panja ndipo anadabwa kwambiri ndi zimene anaona.

Tomoko ananena kuti, “Sindimadziwa kuti mvula yochokera kwa Mulungu, imakulitsa maluwa.”

ZOTI MUCHITE

Mwana wanuyo muwerengereni:

Machitidwe 14:17

Muuzeni mwanayo kuti aloze:

Windo Mbalame Tomoko

Mtengo Maluwa

Pezani zinthu zobisika.

Kachilombo Ndege

Mufunseni mwana wanu kuti:

N’chifukwa chiyani Yehova analenga mvula?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena