Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • wp17 No. 3 tsamba 2
  • Mawu Oyamba

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mawu Oyamba
  • Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawira)—2017
  • Nkhani Yofanana
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
  • Kodi Ulosi wa Anthu 4 Okwera Pamahatchi Umakukhudzani Bwanji Inuyo?
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawira)—2017
  • Anthu 4 Okwera Pamahatchi
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
  • Nkhondo ya ku Ukraine Ikuwonjezera Vuto la Kuchepa Kwa Chakudya Padziko Lonse
    Nkhani Zina
Onani Zambiri
Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawira)—2017
wp17 No. 3 tsamba 2

Mawu Oyamba

KODI INUYO MUKUGANIZA BWANJI?

Ambiri amadziwa ulosi wonena za anthu 4 okwera pamahatchi wopezeka m’buku la Chivumbulutso. Ena amachita mantha akawerenga ulosiwu, pomwe ena umawasangalatsa. Taonani zimene Baibulo limanena zokhudza ulosiwu:

“Wodala ndi munthu amene amawerengera ena mokweza, ndiponso anthu amene akumva mawu a ulosi umenewu.”​—Chivumbulutso 1:3.

Nsanja ya Olonda iyi ikufotokoza kuti ulosi umenewu ndi nkhani yosangalatsa kwa anthufe.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena