Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb17 May tsamba 1
  • Zitsanzo za Ulaliki

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zitsanzo za Ulaliki
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
  • Timitu
  • Nkhani Yofanana
  • NSANJA YA OLONDA
  • KUPHUNZITSA CHOONADI
  • BANJA LANU LIKHOZA KUKHALA LOSANGALALA
  • LEMBANI ULALIKI WANUWANU
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
  • Mawu Oyamba
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawira)—2017
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
mwb17 May tsamba 1
A Mboni za Yehova akugwira ntchito yosamalira Nyumba ya Ufumu

Akukonza Nyumba ya Ufumu ku Switzerland

Zitsanzo za Ulaliki

NSANJA YA OLONDA

Nsanja ya Olonda Na. 3 2017 |Kodi Nkhani ya Anthu 4 Okwera Pamahatchi Ikutikhudza Bwanji?

Mawu Oyamba: M’buku la Chivumbulutso muli ulosi wonena za anthu 4 okwera pamahatchi. Ena amachita mantha akamva ulosiwu pomwe ena amachita nawo chidwi kwambiri.

Lemba: Chiv. 1:3

Perekani Magaziniyo: Nsanja ya Olonda iyi ikufotokoza mmene ulosi wonena za anthu okwera pa mahatchiwa ulili wosangalatsa kwa tonsefe.

KUPHUNZITSA CHOONADI

Baibulo lotsegula

Funso: Kodi mukuganiza kuti n’zotheka anthufe kudziwa zinthu zam’tsogolo?

Lemba: Yes. 46:10

Zoona Zake: Mulungu amatiululira zinthu zam’tsogolo pogwiritsa ntchito Mawu ake, Baibulo.

BANJA LANU LIKHOZA KUKHALA LOSANGALALA

Banja Lanu Likhoza Kukhala Losangalala

Mawu Oyamba: Ndikufuna kukuonetsani kavidiyo kachidule ka nkhani yokhudza banja. [Onetsani vidiyo yothandiza pogawira kabuku kakuti Banja Lanu Likhoza Kukhala Losangalala.]

Perekani Kabuku: Ndingathe kukupatsani kabuku kamene katchulidwa muvidiyoyi ngati mungakonde kapena ndingakusonyezeni mmene mungakapangire dawunilodi pawebusaiti.

LEMBANI ULALIKI WANUWANU

Potengera zitsanzozi, konzani njira imene mungagwiritse ntchito.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena