Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • wp18 No. 3 tsamba 2
  • Mawu Oyamba

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mawu Oyamba
  • Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawira)——2018
  • Nkhani Yofanana
  • Kodi Mulungu Amamva Bwanji Akamakuonani Mukuvutika?
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawira)——2018
Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawira)——2018
wp18 No. 3 tsamba 2

Mawu Oyamba

KODI MULUNGU ZIMAM’KHUDZA MUKAMAVUTIKA?

Pakachitika ngozi komanso anthu akamavutika ndiponso kufa, ambiri amafunsa kuti, ‘Kodi Mulungu amaona zimene zikuchitikazi?’ Baibulo limanena kuti:

“Pakuti maso a Yehova ali pa olungama, ndipo makutu ake amamva pembedzero lawo, koma nkhope ya Yehova imakwiyira anthu ochita zoipa.”​—1 Petulo 3:12.

Nsanja ya Olonda iyi ikufotokoza mmene Mulungu amatithandizira komanso zimene akuchita kuti athetse mavuto onse.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena