Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • wp20 No. 2 tsamba 16
  • Kodi Ufumu wa Mulungu N’chiyani?

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kodi Ufumu wa Mulungu N’chiyani?
  • Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawira)—2020
  • Nkhani Yofanana
  • Ufumu wa Mulungu
    Galamukani!—2013
  • Choonadi Chonena za Ufumu wa Mulungu
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawira)—2020
  • Kodi Ufumu wa Mulungu N’chiyani?
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawira)—2016
  • Kodi Yesu Anaphunzitsa Chiyani za Ufumu wa Mulungu?
    Nsanja ya Olonda—2010
Onani Zambiri
Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawira)—2020
wp20 No. 2 tsamba 16

Kodi Ufumu Wa Mulungu N’chiyani?

Munthu akuwerenga Baibulo atakhala pampando kutsogolo kwa nyumba ya boma.

Anthu ambiri amapemphera kuti Ufumu wa Mulungu ubwere. Koma kodi munadzifunsapo kuti, Kodi Ufumu wa Mulungu n’chiyani komanso udzachita zotani?

TAONANI ZIMENE BAIBULO LIMANENA:

  • Kodi Ufumu wa Mulungu n’chiyani?

    Ndi boma lakumwamba ndipo Yesu Khristu ndi Mfumu yake.​—Yesaya 9:6, 7; Mateyu 5:3; Luka 1:31-33.

  • Kodi Ufumu wa Mulungu udzachita zotani?

    Udzathetsa zoipa zonse ndipo udzabweretsa mtendere wosatha padzikoli.​—Danieli 2:44; Mateyu 6:10.

  • Kodi kufunafuna Ufumu choyamba n’kutani?

    Ndi kukhala kumbali ya Ufumu wa Mulungu komanso kukhulupirira kuti ndi Ufumu wokhawu umene udzakonze zinthu padzikoli kuti zikhale mmene Mulungu amafunira.​—Mateyu 6:33; 13:44.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena