Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb16 April tsamba 4
  • Yobu Sanalole Kuti Maganizo Olakwika Amusokoneze

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Yobu Sanalole Kuti Maganizo Olakwika Amusokoneze
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
  • Nkhani Yofanana
  • Yobu Analemekeza Dzina la Yehova
    Nsanja ya Olonda—2009
  • “Yembekezera Yehova”
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2022
  • Kodi Yobu Anali Ndani?
    Zimene Tingaphunzire Munkhani za M’Baibulo
  • Yobu Anapirira—Nafenso Tingatero!
    Nsanja ya Olonda—1994
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
mwb16 April tsamba 4

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | YOBU 21-27

Yobu Sanalole Kuti Maganizo Olakwika Amusokoneze

Yobu watseka khutu lake

Satana amanena zinthu zabodza pofuna kufooketsa atumiki a Yehova masiku ano. Taonani mfundo zopezeka m’buku la Yobu, zosonyeza kusiyana pakati pa mabodza a Satana ndi mmene Yehova amawonera atumiki ake. Lembani mavesi ena amene amakutsimikizirani kuti Yehova amakuganizirani.

MABODZA OMWE SATANA AMANENA

MMENE YEHOVA AMAONERA ATUMIKI AKE

Mulungu ali ndi mfundo zokhwima ndipo amaona kuti palibe chanzeru chimene atumiki ake angachite. Zolengedwa zake zonse sizingamusangalatse (Yobu 4:18; 25:5)

Yehova amayamikira kwambiri tikamayesetsa kumutumikira modzichepetsa (Yobu 36:5)

Munthu ndi wosafunika kwa Mulungu (Yobu 22:2)

Yehova amasangalala ndiponso amatidalitsa tikamamutumikira mokhulupirika (Yobu 33:26; 36:11)

Mulungu alibe nazo kanthu kuti ndiwe wolungama (Yobu 22:3)

Yehova amasamalira olungama (Yobu 36:7)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena