Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb16 August tsamba 3
  • Pitirizani Kukhala M’malo Otetezeka a Wam’mwambamwamba

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Pitirizani Kukhala M’malo Otetezeka a Wam’mwambamwamba
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
  • Nkhani Yofanana
  • Kupulumutsidwa ku Misampha ya Wosaka Mbalame
    Nsanja ya Olonda—2007
  • Yehova Ndiye Pothaŵirapo Pathu
    Nsanja ya Olonda—2001
  • Chinsinsi Chimene Ufunika Kuuzako Ena
    Nsanja ya Olonda—2010
  • Chinsinsi Chimene Tonsefe Timafuna Titachidziwa
    Phunzitsani Ana Anu
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
mwb16 August tsamba 3

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | MASALIMO 87-91

Pitirizani Kukhala M’malo Otetezeka a Wam’mwambamwamba

Timatetezeka mwauzimu tikakhala “m’malo achitetezo” a Yehova

91:1, 2, 9-14

  • Kuti tikhale m’malo achitetezo a Yehova, timafunika kudzipereka komanso kubatizidwa

  • Anthu amene sakhulupirira Mulungu sadziwa malo amenewa

  • Anthu amene ali m’malo achitetezo a Yehova sakopeka ndi anthu kapena chilichonse chimene chingapangitse kuti asiye kukhulupirira komanso kukonda Mulungu

“Wosaka mbalame” akufunitsitsa kutigwira

91:3

  • Mbalame ndi zochenjera kwambiri, ndipo ndi zovuta kugwira

  • Wosaka mbalame amayang’anitsitsa zimene mbalamezo zimakonda, ndipo amakonza misampha kuti azigwire

  • Nayenso Satana, yemwe ndi “wosaka mbalame,” amayang’anitsitsa zimene atumiki a Yehova amakonda kuchita ndipo amatchera misampha n’cholinga choti awagwire

Mbalame ikuyang’ana msampha, pamene wosaka mbalame akuiyang’anitsitsa ali chapafupi

Misampha 4 yoopsa imene Satana amagwiritsa ntchito kuti atikole:

  • Mkhristu akuthawa anthu amene akumuzunza

    Kuopa Anthu

  • Mulu wa ndalama

    Kukonda Chuma

  • Banja likuchokera kumalo oonetsera zisudzo

    Zosangalatsa Zosayenera

  • Anthu awiri akukangana

    Kusemphana Maganizo ndi Anthu Ena

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena