Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb17 December tsamba 3
  • ‘Gwirani Chovala cha Munthu Amene ndi Myuda’

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • ‘Gwirani Chovala cha Munthu Amene ndi Myuda’
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
  • Nkhani Yofanana
  • Tipita Nanu Limodzi
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2020
  • “Tipita Nanu Limodzi”
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2016
  • “Ana Anu Aamuna ndi Ana Anu Aakazi Adzanenera”
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
  • Oyenerera Kutsogoleredwa ku Akasupe a Madzi a Moyo
    Nsanja ya Olonda—2008
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
mwb17 December tsamba 3
Munthu wagwira chovala cha Myuda

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | ZEKARIYA 1-8

“Gwirani Chovala cha Munthu Amene ndi Myuda”

8:20-23

Amuna 10 ochokera m’zilankhulo zonse za anthu a mitundu ina, adzagwira chovala cha munthu amene ndi Myuda ndi kunena kuti: “Anthu inu tipita nanu limodzi.” M’masiku otsiriza ano, anthu a mitundu yonse akubwera kudzalambira Yehova limodzi ndi Akhristu odzozedwa

Kodi a nkhosa zina amathandiza Akhristu odzozedwa m’njira ziti masiku ano?

  • A Mboni awiri ali mu utumiki

    Amagwira nawo ntchito yolalikira ndi mtima wonse

  • Akuika ndalama m’bokosi la zopereka

    Amathandiza ntchito yolalikira ndi ndalama zawo

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena