Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb19 January tsamba 3
  • Anaimbidwa Mlandu Wosokoneza Anthu Komanso Kuukira Boma

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Anaimbidwa Mlandu Wosokoneza Anthu Komanso Kuukira Boma
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
  • Nkhani Yofanana
  • Paulo Anapempha Kukaonekera kwa Kaisara Ndipo Kenako Analalikira Mfumu Herode Agiripa
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
mwb19 January tsamba 3

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | MACHITIDWE 23-24

Mwana wamwamuna wa mlongo wake wa Paulo akulankhula ndi mkulu wa asilikali

Anaimbidwa Mlandu Wosokoneza Anthu Komanso Kuukira Boma

23:12, 16; 24:2, 5, 6, 10-21

Ayuda a ku Yerusalemu ‘analumbira mochita kudzitemberera’ kuti aphe Paulo. (Mac. 23:12) Komabe chinali cholinga cha Yehova kuti Paulo apite ku Roma kuti akachitirenso umboni kumeneko. (Mac. 23:11) Mwana wamwamuna wa mlongo wake wa Paulo anadziwa za chiwembuchi ndipo anakamuuza. Zimenezi zinathandiza kuti Paulo asaphedwe. (Mac. 23:16) Kodi nkhani imeneyi ikutiphunzitsa chiyani pa nkhani ya . . .

  • zimene anthu ena amachita pofuna kulepheretsa cholinga cha Mulungu?

  • njira zimene Mulungu angagwiritse ntchito potithandiza?

  • kulimba mtima?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena