Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb19 January tsamba 4
  • January 21-27

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • January 21-27
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
mwb19 January tsamba 4

January 21-27

MACHITIDWE 25-26

  • Nyimbo Na. 73 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Paulo Anapempha Kukaonekera kwa Kaisara Ndipo Kenako Analalikira Mfumu Herode Agiripa”: (10 min.)

    • Mac. 25:11​—Paulo anagwiritsa ntchito ufulu wake ndipo anapempha kukaonekera kwa Kaisara (bt 198 ¶6)

    • Mac. 26:1-3​—Paulo anaikira kumbuyo choonadi pamaso pa Mfumu Herode Agiripa (bt 198-201 ¶10-16)

    • Mac. 26:28​—Mfumu Agiripa inakhudzidwa kwambiri ndi zimene Paulo ananena (bt 202 ¶18)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (8 min.)

    • Mac. 26:14​—Kodi chisonga chotosera n’chiyani? (“nyama imene ikuponya miyendo yake kuti imenye zisonga zotosera” mfundo zimene ndikuphunzira pa Mac. 26:14, nwtsty;  matanthauzo a mawu ena, “Chisonga chotosera” nwt)

    • Mac. 26:27​—N’chifukwa chiyani Mfumu Agiripa inakanika kuyankha pamene Paulo anafunsa ngati imakhulupirira mwa aneneri? (w03 11/15 16-17 ¶14)

    • Kodi mwaphunzira zotani zokhudza Yehova pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

    • Kodi ndi mfundo zina ziti zothandiza zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Mac. 25:1-12 (th phunziro 5)

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Vidiyo ya Ulendo Wobwereza Woyamba: (5 min.) Onerani ndi kukambirana mfundo za m’vidiyoyi.

  • Ulendo Wobwereza Woyamba: (Osapitirira 3 min.) Gwiritsani ntchito chitsanzo cha ulendo wobwereza woyamba. (th phunziro 2)

  • Ulendo Wobwereza Woyamba: (Osapitirira 4 min.) Yambani ndi chitsanzo cha ulendo wobwereza woyamba. Musonyezeni buku la Zimene Baibulo Limaphunzitsa. (th phunziro 3)

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 38

  • “Lamulo Lovomereza Ntchito Yathu Yolalikira ku Quebec”: (15 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyoyi.

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) jy mutu 22

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 81 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena