Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 81
  • Moyo wa Mpainiya

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Moyo wa Mpainiya
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Moyo wa Mpainiya
    Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Khalani ndi Moyo Wopambana
    Imbirani Yehova
  • Moyo Ndi Wodabwitsa
    Imbirani Yehova
  • Moyo Ndi Wodabwitsa
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 81

NYIMBO 81

Moyo wa Mpainiya

Losindikizidwa

(Mlaliki 11:6)

  1. 1. Tsiku likayamba, tulo tikukoma

    Timadzuka kupita

    Kolalikira uthenga

    Ndipo Mulungu amatitsogolera.

    Timasangalala

    Anthu akamatimvetsera.

    (KOLASI)

    Tinasankha

    Kutumikira Yehova.

    Timachita zofuna zake.

    Tipitilizabe kulalikiraku.

    Tikatero timasonyeza

    Chikondi.

  2. 2. Pofika madzulo timatopa ndithu

    Komabe timapeza

    Chimwemwe potumikira.

    Yehova Mulungu amatidalitsa.

    Nthawi zonse

    Timamuthokoza potithandiza.

    (KOLASI)

    Tinasankha

    Kutumikira Yehova.

    Timachita zofuna zake.

    Tipitilizabe kulalikiraku.

    Tikatero timasonyeza

    Chikondi.

(Onaninso Yos. 24:15; Sal. 92:2; Aroma 14:8.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena