Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 38
  • Adzakulimbitsa

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Adzakulimbitsa
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Mulungu Adzakupatsani Mphamvu
    Imbirani Yehova
  • Tikhale Ndi Chikhulupiriro Cholimba
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Kukonzekera Kupita Kokalalikira
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Kukonzekera Kupita Kolalikira
    Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 38

NYIMBO 38

Adzakulimbitsa

Losindikizidwa

(1 Petulo 5:10)

  1. 1. Panali chifukwa chimene Mulungu

    Anakupatsira choonadi.

    Anaona mtima wofuna kuchita

    Zabwino zomusangalatsadi.

    Unalonjeza kum’tumikira

    Ndipo iye anakuthandiza.

    (KOLASI)

    Ndi magazi a Yesu

    Anakuwombola.

    Ndiwe wa Mulungu,

    Adzakulimbitsa.

    Adzakutsogolera

    Ndi mzimu woyera.

    Adzakuteteza,

    Adzakulimbitsa.

  2. 2. Mulungu anapereka Mwana wake,

    Amafuna zizikuyendera.

    Ngati mwana wake anakupatsadi

    Sangalephere kukulimbitsa.

    Chikondi chako sangaiwale

    Ndipo sangasiye anthu ake.

    (KOLASI)

    Ndi magazi a Yesu

    Anakuwombola.

    Ndiwe wa Mulungu,

    Adzakulimbitsa.

    Adzakutsogolera

    Ndi mzimu woyera.

    Adzakuteteza,

    Adzakulimbitsa.

(Onaninso Aroma 8:32; 14:​8, 9; Aheb. 6:10; 1 Pet. 2:9.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena