Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb19 June tsamba 4
  • Kodi Maganizo a Yehova Ndi Otani pa Nkhaniyi?

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kodi Maganizo a Yehova Ndi Otani pa Nkhaniyi?
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
  • Nkhani Yofanana
  • Kodi Mumasankha Bwanji Zochita?
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2016
  • N’chiyani Chingatithandize Kuti Tizisankha Zinthu Mwanzeru?
    Mungakhale Ndi Moyo Mpaka Kalekale—Kuphunzira Baibulo Mokambirana
  • Yendani Motsatira Mfundo za Makhalidwe Abwino za Mulungu
    Nsanja ya Olonda—2002
  • Muzikhulupirira Yehova Kuti Muzisankha Zochita Mwanzeru
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2017
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
mwb19 June tsamba 4

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

Kodi Maganizo a Yehova Ndi Otani pa Nkhaniyi?

Tisanasankhe zochita pa nkhani iliyonse, kaya yaikulu kapena yaing’ono, tizidzifunsa kuti, ‘Kodi maganizo a Yehova ndi otani pa nkhaniyi?’ Ngakhale kuti sitingadziwe zonse zokhudza mmene Yehova amaganizira, Mawu ake angatithandize kuti tichite “ntchito iliyonse yabwino.” (2 Tim. 3:16, 17; Aroma 11:33, 34) Yesu ankadziwa bwino zimene Yehova amafuna ndipo ankachita zimenezo pa moyo wake. (Yoh. 4:34) Ifenso tiziyesetsa kutsanzira Yesu posankha zinthu zimene zingasangalatse Yehova.​—Yoh. 8:28, 29; Aef. 5:15-17.

ONERANI VIDIYO YAKUTI PITIRIZANI KUZINDIKIRA CHIFUNIRO CHA YEHOVA (LEV. 19:18), KENAKO YANKHANI MAFUNSO OTSATIRAWA:

  • N’chifukwa chiyani tiyenera kugwiritsa ntchito mfundo za m’Baibulo pa moyo wathu?

  • Kodi muyenera kuganizira mfundo za m’Baibulo ziti mukamasankha nyimbo?

  • Kodi muyenera kuganizira mfundo za m’Baibulo ziti pa nkhani ya zovala komanso kudzikongoletsa?

  • Kodi ndi pa nkhani zinanso ziti pomwe tingafunike kugwiritsa ntchito mfundo za m’Baibulo?

  • Kodi tingatani kuti tizidziwa bwino zimene Yehova amafuna kuti tizichita?

Achinyamata a Mboni ochokera m’mayiko osiyanasiyana akujambulitsa atavala zovala zamitundumitundu

Zimene timasankha zimasonyeza mmene ubwenzi wathu ndi Yehova ulili

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena