Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb19 September tsamba 2
  • “Wansembe Mpaka Muyaya Monga mwa Unsembe wa Melekizedeki”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Wansembe Mpaka Muyaya Monga mwa Unsembe wa Melekizedeki”
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
  • Nkhani Yofanana
  • Mafunso Ochokera kwa Oŵerenga
    Nsanja ya Olonda—1993
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
mwb19 September tsamba 2
Yesu wakhala pampando wake wachifumu kumwamba ndipo wagwira ndodo m’dzanja lake

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | AHEBERI 7-8

“Wansembe Mpaka Muyaya Monga mwa Unsembe wa Melekizedeki”

7:1-3, 17

N’chifukwa chiyani tinganene kuti Melekizedeki ankaimira Yesu?

  • 7:1​—Anali mfumu komanso wansembe

  • 7:3, 22-25​—Palibe pomwe pamasonyeza kuti analowa m’malo kapenanso kulowedwa m’malo ndi munthu wina

  • 7:5, 6, 14-17​—Anachita kusankhidwa kuti akhale wansembe, osati chifukwa chobadwira m’banja la ansembe

Mkulu wa ansembe wavala chovala chake cha unsembe

Kodi unsembe wa Khristu umaposa bwanji wa Aroni? (it-1 1113 ¶4-5)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena