Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb19 September tsamba 2
  • September 2-8

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • September 2-8
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
mwb19 September tsamba 2

September 2-8

AHEBERI 7-8

  • Nyimbo Na. 16 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Wansembe Mpaka Muyaya Monga mwa Unsembe wa Melekizedeki”: (10 min.)

    • Aheb. 7:1, 2​—Melekizedeki yemwe anali mfumu komanso wansembe anakumana ndi Abulahamu n’kumudalitsa (it-2 366)

    • Aheb. 7:3​—Melekizedeki analibe “mzere wa mibadwo ya makolo” ndipo anakhala “wansembe kwamuyaya” (it-2 367 ¶4)

    • Aheb. 7:17​—Yesu ndi “wansembe mpaka muyaya monga mwa unsembe wa Melekizedeki” (it-2 366)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (8 min.)

    • Aheb. 8:3​—Kodi pali kusiyana kotani pakati pa mphatso ndi nsembe zomwe anthu ankapereka malinga ndi Chilamulo cha Mose? (w00 8/15 14 ¶11)

    • Aheb. 8:13​—Kodi pangano la Chilamulo linakhala bwanji “lotha ntchito” m’nthawi ya Yeremiya? (it-1 523 ¶5)

    • Kodi mwaphunzira zotani zokhudza Yehova pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

    • Kodi ndi mfundo zina ziti zothandiza zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Aheb. 7:1-17 (th phunziro 5)

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Kuwerenga Komanso Kuphunzitsa Mwaluso: (10 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyo yakuti Kugwiritsa Ntchito Bwino Zinthu Zooneka, kenako kambiranani phunziro 9 m’kabuku ka Kuphunzitsa.

  • Nkhani: (Osapitirira 5 min.) it-1 524 ¶3-5​—Mutu: Kodi Pangano Latsopano N’chiyani? (th phunziro 7)

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 124

  • Zimene Gulu Lathu Lachita: (15 min.) Onerani vidiyo ya Zimene Gulu Lathu Lachita ya September. Limbikitsani abale ndi alongo kuti ngati angathe akaone malo ku ofesi ya nthambi kapena kulikulu lathu lapadziko lonse.

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) jy mutu 49

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 70 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena