Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb19 October tsamba 4
  • “Mapeto a Zinthu Zonse Ayandikira”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Mapeto a Zinthu Zonse Ayandikira”
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
  • Nkhani Yofanana
  • Kuchereza Alendo Ndi Kofunika Kwambiri
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2018
  • ‘Cherezani Alendo’
    Nsanja ya Olonda—1996
  • Kodi Tingatani Kuti Tizikondana Kwambiri?
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2023
  • Tizichitira Ena “Zabwino” Pokhala Ochereza (Mat. 12:35a)
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
mwb19 October tsamba 4

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | 1 PETULO 3-5

“Mapeto a Zinthu Zonse Ayandikira”

4:7-9

M’bale wachinyamata wakhala pasofa ndipo akupemphera

Posachedwapa chisautso chachikulu chomwe sichinayambe chachitikapo, chiyamba. Kodi tingatani kuti tilimbitse chikhulupiriro chathu panopa nthawiyi isanafike?

  • Tizipemphera nthawi zonse pogwiritsa ntchito mitundu yonse ya pemphero

  • Tizikonda abale ndi alongo athu ndipo tiziyesetsa kuchita zinthu mogwirizana kwambiri

  • Tizikhala ochereza

Banja likuthandiza bambo wina ndi ana ake awiri powapatsa zakudya komanso zovala; a Mboni za Yehova akukonza denga la nyumba yomwe yawonongeka kutachitika chimphepo

DZIFUNSENI KUTI, ‘Kodi ndi njira zina ziti zomwe ndingasonyezere kuti ndimakonda kwambiri abale, nanga ndingasonyeze bwanji mtima wochereza kwa abale ndi alongo a m’dziko lathu komanso ochokera m’mayiko ena?’

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena