Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb20 May tsamba 2
  • Yosefe Anachitiridwa Nsanje

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Yosefe Anachitiridwa Nsanje
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
  • Nkhani Yofanana
  • Chikondi Chimagonjetsa Nsanje Yoipa
    Nsanja ya Olonda—1995
  • Nsanje ya pa Kulambira Yehova Koyera
    Nsanja ya Olonda—1995
  • Zimene Muyenera Kudziŵa Ponena za Nsanje
    Nsanja ya Olonda—1995
  • Kodi Akristu Ayenera Kukhala Ansanje?
    Nsanja ya Olonda—2002
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
mwb20 May tsamba 2
Azichimwene ake a Yosefe akumukankhira ku chitsime chopanda madzi. Mchimwene wake wina wanyamula mkanjo wapadera wa Yosefe.

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | GENESIS 36-37

Yosefe Anachitiridwa Nsanje

37:3-9, 11, 23, 24, 28

Zimene zinachitikira Yosefe zikusonyeza zinthu zoipa zomwe zimachitika chifukwa cha nsanje yosayenera. Gwirizanitsani malemba ndi zifukwa zomwe zili m’munsimu zotichititsa kuthetsa maganizo alionse a nsanje yosayenera omwe tingakhale nawo.

LEMBA

  • 1 Sam. 18:8, 9

  • Miy. 14:30

  • 2 Akor. 12:20

  • Agal. 5:19-21

CHIFUKWA

  • Anthu a nsanje sadzalowa mu Ufumu wa Mulungu

  • Nsanje imasokoneza mtendere ndi mgwirizano mumpingo

  • Nsanje imativulaza

  • Nsanje imatilepheretsa kuona zabwino mwa anthu ena

Kodi ndi zinthu ziti zomwe zingatichititse kuti tiyambe kuchita nsanje?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena