Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb20 June tsamba 7
  • “Ine Ndidzakhala Nawe Polankhula”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Ine Ndidzakhala Nawe Polankhula”
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
  • Nkhani Yofanana
  • “Musamade Nkhawa ndi Kanthu Kalikonse”
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
  • Tsanzirani Chikhulupiriro cha Mose
    Nsanja ya Olonda—2014
  • Phunzirani Njira za Yehova
    Nsanja ya Olonda—2005
  • Mmene Moyo wa Mose Umakukhudzirani
    Galamukani!—2004
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
mwb20 June tsamba 7
Mose ndi Aroni akulankhula pamaso pa Farao ndi anthu ena a m’nyumba yachifumu.

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | EKISODO 4-5

“Ine Ndidzakhala Nawe Polankhula”

4:10-15

Yehova anathandiza Mose kuti asiye kuchita mantha. Kodi tingaphunzire chiyani kuchokera pa zimene Yehova anauza Mose?

  • Tizipewa mtima wodzikayikira

  • Tizidalira Yehova kuti akhoza kutipatsa chilichonse chomwe tingafune kuti tikwanitse utumiki wathu

  • Kukhulupirira Mulungu kungatithandize kuti tisamaope anthu

M’bale akufotokoza zimene amakhulupirira kwa akuluakulu a khoti.

Kodi Yehova wandithandiza bwanji kuthana ndi mavuto pogwira ntchito yolalikira?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena