Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb20 August tsamba 7
  • Mmene Malamulo 10 Amakukhudzirani

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mmene Malamulo 10 Amakukhudzirani
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
  • Nkhani Yofanana
  • Kodi Malamulo Khumi a Mulungu Ndi Chiyani?
    Kuyankha Mafunso a M’Baibulo
  • Kodi Ndimotani Mmene Mumawonera Malamulo Khumi?
    Nsanja ya Olonda—1989
  • Kodi Ife Tiri Pansi pa Malamulo Khumi?
    Mungathe Kukhala ndi Moyo Kosatha m’Paradaiso pa Dziko Lapansi
  • Kodi Malamulo Khumi Amatanthauzanji kwa Inu?
    Nsanja ya Olonda—1989
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
mwb20 August tsamba 7
Mose waima patsogolo pa phiri la Sinai, ndipo watenga miyala iwiri yokhala ndi Malamulo 10.

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | EKISODO 19-20

Mmene Malamulo 10 Amakukhudzirani

20:3-17

Akhristu satsatira Chilamulo cha Mose. (Akl 2:13, 14) Ndiye kodi Malamulo 10 komanso Chilamulo chonse zili ndi phindu lililonse kwa ife masiku ano?

  • Amasonyeza mmene Yehova amaonera zinthu

  • Amasonyeza zimene Yehova amayembekezera kuti tizichita

  • Amasonyeza mmene tiyenera kuchitira zinthu ndi anthu anzathu

Kodi Malamulo 10 amakuphunzitsani chiyani za Yehova?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena