Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb20 September tsamba 6
  • Chopereka kwa Yehova

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Chopereka kwa Yehova
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
  • Nkhani Yofanana
  • Dipatimenti Yoona za Mapulani ndi Zomangamanga Padziko Lonse
    Buku Lapachaka la Mboni za Yehova la 2015
  • Ntchito Yomanga Yomwe Imalemekeza Yehova
    Ufumu wa Mulungu Ukulamulira
  • Tizilemekeza Malo Athu Olambirira Yehova
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
  • Mmene Anthu Akuwonjezekera Pakufunika Nyumba Zina Mwamsanga
    Nsanja ya Olonda—2002
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
mwb20 September tsamba 6
M’bale akuponya ndalama m’bokosi la zopereka.

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | EKISODO 29-30

Chopereka kwa Yehova

30:11-16

Pamene chihema chinkamangidwa, anthu onse, kaya olemera kapena osauka, anali ndi mwayi wopereka ndalama zothandizira pa kulambira Yehova. Kodi masiku ano tingapereke bwanji kwa Yehova? Njira imodzi ndi kupereka ndalama zothandizira pomanga kapena kukonza Nyumba za Ufumu, Malo a Misonkhano, maofesi a omasulira mabuku, nyumba za Beteli kapena nyumba zina zimene zimagwiritsidwa ntchito polambira Yehova.

Kodi malemba otsatirawa amatiphunzitsa chiyani pa nkhani yopereka ndalama zothandizira pa kulambira koona?

  • 1Mb 29:5

  • Mko 12:43, 44

  • 1Ak 16:2

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena