Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb20 December tsamba 6
  • Kodi Tsiku la Mwambo Wophimba Machimo Limakukhudzani Bwanji?

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kodi Tsiku la Mwambo Wophimba Machimo Limakukhudzani Bwanji?
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
  • Nkhani Yofanana
  • Kufukiza Kodi N’kofunika pa Kulambira Koona?
    Nsanja ya Olonda—2003
  • Zimene Tingaphunzire M’buku la Levitiko
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2019
  • Mmene Tingam’fikire “Wakumva Pemphero”
    Nsanja ya Olonda—2006
  • Maguwa Ansembe a Chihema Anali Ofunika pa Kulambira Koona
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
mwb20 December tsamba 6
Mkulu wansembe akulowa m’Malo Oyera Koposa atanyamula zofukiza ndi makala a moto.

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | LEVITIKO 16-17

Kodi Tsiku la Mwambo Wophimba Machimo Limakukhudzani Bwanji?

16:12-15

Kodi tikuphunzira chiyani pa mmene ansembe ankagwiritsira ntchito zofukiza pa Tsiku la Mwambo Wophimba Machimo?

  • Mapemphero ovomerezeka a atumiki okhulupirika a Yehova ali ngati zofukiza. (Sl 141:2) Mkulu wa ansembe ankapereka zofukiza kwa Yehova mwaulemu kwambiri. Ifenso tikamapemphera kwa Yehova tiyenera kusonyeza kuti timamulemekeza kwambiri

  • Mkulu wa ansembe ankafunika kuika zofukiza pamoto asanapereke nsembe. Mofanana ndi zimenezi, Yesu asanapereke nsembe yake anafunika kusonyeza kuti anali wokhulupirika. Izi zinathandiza kuti Yehova alandire nsembe yakeyo

Zithunzi: 1. Banja likupemphera litamaliza kukonzekera utumiki. 2. Banja lomwe lija likulalikira kwa dalaiva pogwiritsa ntchito tabuleti.

Kodi ndingatani kuti nsembe zanga zikhale zovomerezeka kwa Yehova?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena