Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb21 January tsamba 8
  • Chaka cha Ufulu Komanso Ufulu Womwe Tidzakhale Nawo M’tsogolo

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Chaka cha Ufulu Komanso Ufulu Womwe Tidzakhale Nawo M’tsogolo
  • Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
  • Nkhani Yofanana
  • Yehova Anakonza Zoti Tikhale ndi Ufulu
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2019
  • Chaka Choliza Lipenga cha Yehova—Nthawi Yathu Yakusangalala
    Nsanja ya Olonda—1987
  • Mafunso Ochokera kwa Oŵerenga
    Nsanja ya Olonda—2004
  • Chaka Choliza Lipenga cha Akristu Chifika Pachimake mu Zaka Chikwi
    Nsanja ya Olonda—1987
Onani Zambiri
Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
mwb21 January tsamba 8

Aisiraeli omwe anali akapolo akubwerera kwawo m’Chaka cha Ufulu

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Chaka cha Ufulu Komanso Ufulu Womwe Tidzakhale Nawo M’tsogolo

Chaka cha Ufulu chinkathandiza Aisiraeli kuti asamakhale ndi ngongole yosatha komanso asamakhale osauka mpaka kalekale (Le 25:10; it-1 871; onani chithunzi chapachikuto)

Malo ankagulitsidwa potengera kuchuluka kwa zokolola zomwe wogulayo adzapeze pamalowo (Le 25:15; it-1 1200 ¶2)

Yehova ankadalitsa anthu ake akamamvera lamulo lokhudza Chaka cha Ufulu (Le 25:​18-22; it-2 122-​123)

Posachedwapa, anthu okhulupirika adzasangalala ndi madalitso onse a Chaka cha Ufulu chophiphiritsa akadzamasulidwa ku uchimo ndi imfa.​—Aro 8:21.

Anthu akukonza dziko lapansi kukhala paradaiso. 1. Akuchotsa zinyalala. 2. Akumanga nyumba ndi tinjira. 3. Akulima minda ya maluwa.

Kodi tingatani kuti tidzapeze ufulu umene Yehova walonjeza?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena